1001734645

Wolemba: Racheal Julaye.

Nduna ya zokopa alendo Vera Kamtukule yalowa mchipani cha Malawi Congress.

Kamtukule akuchokera ku chipani Cha UTM chomwe chatuluka mu mgwilizano wa Tonse sabata zingapo zapitazo.

Polankhula atalandilidwa mchipanichi, Kamtukule ati iwo aganiza zolowa mchipanichi pofuna kuthandizana ndi President Chakwera kukweza Malawi.

Masiku apitawo Kamtukule anauza nyumba zina zoulutsa mau kuti iye akufuna kutumikila a Malawi ndipo kutuluka kwa chipani cha UTM mu mgwilizano wa Tonse sizikusintha ganizoli.

Oscar Taulo yemwe anali mlangizi wa za malamulo mchipani cha DPP naye walowa mchipani cha MCP.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

See also  Kalindekafe Appointed Inaugural NAMICO Chief

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *