Malawi Freedom Network
Giving you daily news that rock the world
ExclusiveSports

‘A Malawi Musadandaule Taika chidwi pa world cup’_ watero Mabedi

Mphuzitsi wa timu ya mpira wamiyendo yadziko lino Patrick Mabedi wati tsopano agwilitsa ntchito masewela omwe atsala odzigulira malo mumpikisano wa Afcon ngati mbali yokozekela masewera odzigulira malo mumpikisano wapadziko lonse a World Cup.

A Mabedi ayankhula izi kutsatira pomwe timuyi yalephera kudzigulira malo mu mipikisano wa AFCON kutsatila kugonja ndi team ya Senegal 1-0 pamasewero omwe anachitika lero pabwalo la zamasewero la Bingu mu mzinda wa Lilongwe.

Malingana ndi a Mabedi ati timu yadziko linoyi siikuchita bwino kaamba kosakozekera bwino kotero masewero omwe atsalawa apeleka danga lokoza pomwe pakumavunda khola cholinga choti timuyi iyambe kuchita bwino.

Pakadali pano Flames ili pansi penipeni pa gulu L ndipo ilibe ngakhale point ndiimodzi yomwe kuchoka mumasewero anayi omwe yasewera.

Related posts

Dan Lu Loses 12,000 Facebook Followers After Joining MCP

By Burnett Munthali

Analysis: A contrast of leadership styles at the 79th UNGA

Malawi Freedom Network

Chakwera, MCP to lose 2025 Elections — EIU

Malawi Freedom Network

Dzaleka refugee camp Is a hub for human trafficking

By Suleman Chitera

I Can’t Resign – Mabedi

Malawi Freedom Network

Gwengwe tours Pharmavova Malawi Limited in Blantyre

Malawi Freedom Network

Leave a Comment

Leave a review

This website uses cookies to improve your experience. We'll assume you're ok with this, but you can opt-out if you wish. Accept Read More