Ma Banki apeza phindu lochuluka

Ma Banki asanu ndi atatu a m’dziko muno apanga phindu lokwana K256.7 billion m’chaka cha 2023 chokha, boma litadulapo kale msonkho.

Izi ndi malingana ndi lipoti la m’mene chuma chikuyendera m’dziko muno lochokera ku banki yayikulu pa dziko lonse (World Bank).

Lipotili lati phinduli lakwera kuchoka pa K170.8 billion lowe ma banki-wa anapeza m’chaka cha 2022.

Bankiyi yati ngakhale chuma cha dziko lino chakumana ndi mavuto ambiri, gawo la mabanki likupitilira kukwera komanso kupeza  phindu lochuluka.

Related Posts
Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Zuneth Sattar Is An Experienced Property Investor

PROPERTY INVESTOR PROPERTY MARKET AN OVERVIEW This blog will cover a wide range of topics and subjects that relate to Sattar’s Read more

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window