Mwamuna Aliyense Akwatire Akazi Asanu– Swaziland

Mfumu Swati yachitatu mdziko la Swaziland yapereka lamulo loti mwamuna aliyense akuyenera kukwatira akazi osachepera asanu mdzikolo apo biii apite ku ndende.

Malingana ndi uthenga omwe mfumuyi yatulutsa, boma lake ndi lomwe lidzalipira zonse pa nkhani ya mwambo wabanja komaso kugula nyumba zamabanjawo.

Mfumu Mswati yachenjeza kuti yense onyozera alandira chilango chokhwima.

Mfumuyi yati ikukhulupirira kuti izi zithandiza kuti akazi ambiri asakhale pamphala potengera kuti chiwerengero cha akazi nchochuluka poyerekezera ndi amuna

Kuonjezera apo boma la mfumu Mswati lapereka mwayi kwa amuna ochokera mmayiko ena maka a Kummwera kwa Africa kuti ngati angakonde apite mdzikolo kukakwatira akaziwa ndipo adzapatsidwa mwayi okhala nzika za dzikolo.

Mfumu Mswati mwiniyo ali ndi akazi khumi ndi asanu (15) pomwe bambo ake, omwe iyo idawalowa mmalo, adali ndi akazi 70.

Related Posts

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

Martha Chizuma left in the cold as British NCA backtracks on illegal operations in Malawi

By Attwel Chilangambwa After using the embattled Anti-Corruption Bureau (ACB) Director General Martha Chizuma for illegal entry into Malawi, British Read more

British businessman Zuneth Sattar ready to stand trial over Malawi corruption case

BLANTYRE – Businessman Zuneth Sattar, says he is ready to stand before the court of law and prove his innocence Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window