Malawi Freedom Network
Giving you daily news that rock the world
FeaturedSports

titha Kutembenuza Tebulo

Timu ya Civo United yati ili ndi kuthekera kodzidzimutsa timu ya FCB Nyasa Big Bullets nkuitulutsa mu mpikisano wa Airtel Top 8 pa masewero omwe alipo masanawa pa bwalo la Civo.

Mphunzitsi wa timuyi Abas Makawa wati anyamata ake akonzeka ndipo otsatira timuyi abwere adzaone chipambana chawo.

Koma ku mbali ya timu ya FCB Nyasa Big Bullets, Callisto Pasuwa wati akudziwa bwino lomwe mphamvu ya timu ya Civo ndipo akudziwa bwino mothanirana nayo.

Awa ndi masewero achibwereza ndipo matimu awiriwa atakumana koyamba pa bwalo la Kamuzu, Bullets idapambana 2-0.

Wopambana masewerowa akuyembekezeka kukumana ndi wopambana pakati pa Kamuzu Barracks ndi Chitipa United omwe akumane mawa, masewero womwe Chitipa United ikutsogola 2-0 kuchokera m’masewero woyamba.

Related posts

DPP Youth Leader Norman Chisale Criticizes MCP’s Richard Chimwendo Banda Over Response to Police Assault Case

By Suleman Chitera

Hansi Flick not convinced by 18-year-old Barcelona starlet who debuted under Xavi

Malawi Freedom Network

Thrilling and Joyous Mood Engulfs BICC as The Harps Launch ‘Kwa Ife Ayi’ Album

By Burnett Munthali

Daudi advocates for meaningful collaboration

By Suleman Chitera

Education Stakeholders in Mwanza Highlight Resource Shortages as Key Cause of Poor Exam Performance

By Suleman Chitera

Mtetemera retains Creck’s coach role

Malawi Freedom Network

Leave a Comment

* By using this form you agree with the storage and handling of your data by this website.

Leave a review

This website uses cookies to improve your experience. We'll assume you're ok with this, but you can opt-out if you wish. Accept Read More