750 Million Kwacha Siidabwezedwe Ku Dziko Lino

Wapampando wa komiti ya za ulimi ku nyumba ya malamulo a Sameer Suleman wati ndi zomvetsa chisoni kuti a ndale ena amalowetsa ndale pa nkhani zofunikira zokhudza a Malawi.

Iwo amayankhula izi pomwe zotsatira za kafukufuku yemwe boma linakhazikitsa kuti lipeze kuti nkhani yokhudza ndalama yokwana 750 million kwacha yomwe idaperekedwa ku butchala ina yakunja kuti ibweretse fetereza m’dziko muno ili pati.

Iwo ati sipakuoneka chidwi chofuna kulondoloza za ndalamayi zomwe zikupereka chithunzi thunzi kuti nkutheka a ndale ena adapindulapo.

Nduna ya kale ya za ulimi a Robin Lowe adavomereza kuti undunawu udapereka ndalamazi ku kampani yakunjayi kuti ibweretse fetereza yemwe adali wa mu ndondomeko ya AIP koma zidadziwika kuti kampaniyo
Kulibeko.

Pakadali pano a Malawi ambiri adataya mtima kuti ndalama-yi idzabwezedwa.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window