Tue. Apr 30th, 2024

NDIKUFUNA NANKHUMWA AZIMUGWADIRA MUTHARIKA-Namalomba

By ADMIN Mar14,2022

Mneneri wa Chipani cha DPP a Shadreck Namalomba,awunza Kondwani Nankhumwa kuti asamapange ziganizo payekha akafuna kuchita zinthu.

A Namalomba ati,Nankhumwa akamafuna kuchita chinthu chokhuzana ndi mu chipani cha DPP, aziyamba amufusa kale mtsogoleri wa Chipanichi a Mutharika kamba koti iye ndi wamkulu.

Namalomba amalankhula izi ku mkumano womwe udaliko dzulo ku Mangochi.

A Namalomba ,awunza anthu kuti a Nankhumwa ndi munthu wotsokoneza mu chipani ndipo Peter Mutharika,ndiwokhumudwa ndi zomwe Nankhumwa akuchita.“`

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

By ADMIN

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open