Zadziwika kuti mphunzitsi wa Flames, Mario Marinica amalandira pafupifupi K13 million kwacha pa mwezi pomwe mphunzitsi wakale wa timuyi, Meck Mwase ankalandira K1.3 million.
Read also: DPP and AFORD forge ahead with joint manifesto and campaign launch in Blantyre
Read also: FAM, SULOM Bury Hatchet, Pledge United Front for Malawi Football
Maganizo anu ndi otani pa momwe bungwe la Football Association of Malawi-FAM komanso boma amayendetsera bwanji nkhani za ma contract a aphunzitsi a Flames? Tinene kuti vuto ndi aphunzitsi a m’dziko muno?

Read also: Stay Hydrated This Summer: The Healthy Way
Read also: Journalists encouraged to raise awareness on mental health
Read also: The Greed of Dalitso Kabambe: A Child in Politics





