Kwimbi la Asilamu lasonkhana kuchita mapemphero pa bwalo la sukulu ya Mufti Abbassi ku Mangochi pambuyo pakutsiliza kusala kudya kwa masiku asanu ndi anayi.

Munyengoyi, asilamu amapha nyama ndikugawila anthu ena osowa, ngati njira imodzi yochita zachifundo.
Eid Mubarak iyi ndiyosiyanilapo ndi ija magulu ena a Chisilamu amasemphana pa tsiku lomwe mwezi waonekela.
Sponsored • Malawi Freedom Network
MALAWI
FREEDOM
NETWORK
United for Freedom, Justice and a Better Malawi
Airtel Money
0994095804
Mpamba
0881428759
BANK TRANSFER
FDH Bank
Acc No:
1400000670385NBS Bank
Acc No:
10118988Thank you for your support!