Kwimbi la Asilamu lasonkhana kuchita mapemphero pa bwalo la sukulu ya Mufti Abbassi ku Mangochi pambuyo pakutsiliza kusala kudya kwa masiku asanu ndi anayi.

Munyengoyi, asilamu amapha nyama ndikugawila anthu ena osowa, ngati njira imodzi yochita zachifundo.
Read also: World Bank pushes for stronger Land rights amid Malawi’s mining surge
Read also: WOLREC and WUSC Launch Three-Year Initiative to Empower Women and Improve Early Childhood Education
Eid Mubarak iyi ndiyosiyanilapo ndi ija magulu ena a Chisilamu amasemphana pa tsiku lomwe mwezi waonekela.
Read also: Bullets in second FDF final in two years
Read also: Carvajal talks Mbappe, Vinicius, Rodrygo, Kroos, Yamal, Perez, Real Madrid future
Read also: MACRA TO SMOKE OUT MOBILE MONEY FRAUDSTERS





