Chipani chatsopano Cha N D P Achikhazikitsa Mdzikolino

Chipani chatsopano chomwe akuchitcha National Development Party (NDP) ndipo mtsogoleri wake ndia Frank Mwenefumbo achikhazikitsa mdzikolino.

Ofesi ya mkulu oona zakalembera wa zipani zandale yapeleka kale chilolezo ku chipanichi kuti chitha kuyamba kugwira ntchito zake mdzikolino kuyambira pa 1 March, 2024.

Mlembi wamkulu wachipanichi a Gerald Chilongo watsimikiza lero kuti chipanichi achikhazikitsa mwazina pofuna kugwira ntchito ndi a Malawi polimbana ndimavuto monga a zachuma komanso kusakazika kwa zachilengedwe.

Komabe a Chilongo ati pakadalipano chipanichi chaika chidwi polimbikitsa nthambi zake ndipo pakadalipano sichidapange chiganizo ngati chizapange mgwilizano ndi zipani zina kapena ayi.

Mtsogoleri wachipanichi a Mwenefumbo, anakhalapo mneneri wachipani cha UTM.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Biography Of Zuneth Sattar

Zuneth Sattar Director of Xaviar Limited and Xaviar Investments Limited Zuneth Sattar is an experienced and knowledgeable property investor. With Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window