Tikuchosani Ku Bagamoyo Chaka Cha Mawa

Chipani cha DPP chati chikubweleraso m’boma chaka cha mawa kuti chiwombole anthu pa mavuto.

Mkulu owona zokopa anthu m’chipanichi a Everton Chimulirenji ayankhula izi la mulungu pa msonkhano omwe chipanichi chinachititsa ku Ntcheu.

A Chimulirenji ati a Malawi akudutsa mu nyengo zowawa kuphatikizapo njala ndi kukwera mitengo kwa zinthu.

Iwo ati chipanichi chakonzeka kuwaombola a Malawi pa mavutowa kaamba koti mayankho a Malawi ali ndi chipanichi.

Pa msonkhanowu, chipanichi chinalandiraso m’modzi mwa anthu omwe awonetsa chidwi chodzaimira pa mpando wa phungu wa chipanichi m’bomali a Mandela Ndilinde Gomeza.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

David Bisnowaty former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country

Political cum and former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country https://youtu.be/S20UYlVcHs8

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window