Sat. Apr 27th, 2024

Tikuchosani Ku Bagamoyo Chaka Cha Mawa

Chipani cha DPP chati chikubweleraso m’boma chaka cha mawa kuti chiwombole anthu pa mavuto.

Mkulu owona zokopa anthu m’chipanichi a Everton Chimulirenji ayankhula izi la mulungu pa msonkhano omwe chipanichi chinachititsa ku Ntcheu.

A Chimulirenji ati a Malawi akudutsa mu nyengo zowawa kuphatikizapo njala ndi kukwera mitengo kwa zinthu.

Iwo ati chipanichi chakonzeka kuwaombola a Malawi pa mavutowa kaamba koti mayankho a Malawi ali ndi chipanichi.

Pa msonkhanowu, chipanichi chinalandiraso m’modzi mwa anthu omwe awonetsa chidwi chodzaimira pa mpando wa phungu wa chipanichi m’bomali a Mandela Ndilinde Gomeza.

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

Navicha appointed as a leader of opposition in parliament

Member of parliament for Thyolo Thava, Mary Thom Navicha has been recently appointed as a new leader of opposition following Read more

Jumah says it is possible to change Malawi in 10-15 years

By Vincent Gunde President and Commander in Chief of Muvi wa Chilungamo Revolutionary Party (MRP) Bantu Saunders Jumah, says it Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open