Tue. Apr 23rd, 2024

Kwavuta:Nkokenkoke Pa Nkhani Ya Buluma

Mlangizi wa boma pa nkhani za malamulo Thabo Chakaka Nyirenda wasemphana zochita ndi komiti ya Public Appointments-PAC pa nkhani yoti yemwe adali wachiwiri kwa mkulu wa NOCMA, mai Hellen Buluma akaonekere ku nyumbayi kuti akafotokoze mwatchutchutchu zomwe adalemba mu kalata yawo yosiya ntchito.

Mwa zina, a Buluma adati wapampando wa board ya NOCMA yemwenso ndi mlembi mu ofesi ya mtsogoleri wa dziko ndi nduna zake, mai Colleen Zamba, akuluakulu ena a chipani cha MCP komanso a boma ankawakakamiza kuti adzipereka ma contract mwachinyengo.

Koma a Chakaka Nyirenda auza Sipikala wa nyumba ya malamulo, Catherine Gotani Hara kuti a Buluma komanso a Zamba asawonekere ku komiti-yi pomwe PAC yati ipitilira ndi ganizo lake lofunsa awiriwa.

Kodi nkoyeneradi kuti mai Buluma ndi mai Zamba ayankhe mafunso?

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open