Sat. Apr 27th, 2024

Mitawa Ayima Opanda Opikisana Naye

Ogwilizira mpando wa mtsogoleri wa bungwe la Super League of Malawi(Sulom), Colonel Gilbert Mitawa ayimira pa mpando wa mtsogoleri wa bungweri opanda opikitsana nawo.

Izi zikutsatira chikalata chomwe atulutsa a Crowe Howarth Malawi omwe amayendetsa ndondomeko yolandila ma kalata a anthu ofuna kuzayimila pa maudindo ku bungwe la Sulom omwe anatseka kulandila ma kalatawa.

A Mitawa omwe amagwilizira udindo’wu kutsatira kwa kuchoka kwa Fleetwood Haiya amene pano ndi mtsogoleri wa bungwe la Football Association of Malawi akuyembekezeka kupitiliza ngodya zomwe anasiya a Haiya zofuna kusintha mpira.

Pa udindo wa mamembala a komiti yayikulu ya bungweri pali anthu atatu omwe akupikisana omwe ali Isaac Mdindo, William Nhlane ndi Charles Manyungwa.

Zisankho zizachitika pa 30 March, 2024 mu mzinda wa Lilongwe.

Related Posts
I am not a crook— Mulli

MAINTAINED THAT PROCEDURES WERE FOLLOWED—Mulli— Picture by Catherine Maulidi Businessperson and National Bus Services Chairperson Leston Mulli on Tuesday told Read more

Navicha appointed as a leader of opposition in parliament

Member of parliament for Thyolo Thava, Mary Thom Navicha has been recently appointed as a new leader of opposition following Read more

Jumah says it is possible to change Malawi in 10-15 years

By Vincent Gunde President and Commander in Chief of Muvi wa Chilungamo Revolutionary Party (MRP) Bantu Saunders Jumah, says it Read more

Chimulambe says access to clean water is catalyst for socio-economic development

By Vincent Gunde Principal Secretary for Water and Sanitation Ministry Elias Chimulambe, says access to clean and reliable water is Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open