Thu. May 2nd, 2024

Mwamuna Aliyense Akwatire Akazi Asanu– Swaziland

Mfumu Swati yachitatu mdziko la Swaziland yapereka lamulo loti mwamuna aliyense akuyenera kukwatira akazi osachepera asanu mdzikolo apo biii apite ku ndende.

Malingana ndi uthenga omwe mfumuyi yatulutsa, boma lake ndi lomwe lidzalipira zonse pa nkhani ya mwambo wabanja komaso kugula nyumba zamabanjawo.

Mfumu Mswati yachenjeza kuti yense onyozera alandira chilango chokhwima.

Mfumuyi yati ikukhulupirira kuti izi zithandiza kuti akazi ambiri asakhale pamphala potengera kuti chiwerengero cha akazi nchochuluka poyerekezera ndi amuna

Kuonjezera apo boma la mfumu Mswati lapereka mwayi kwa amuna ochokera mmayiko ena maka a Kummwera kwa Africa kuti ngati angakonde apite mdzikolo kukakwatira akaziwa ndipo adzapatsidwa mwayi okhala nzika za dzikolo.

Mfumu Mswati mwiniyo ali ndi akazi khumi ndi asanu (15) pomwe bambo ake, omwe iyo idawalowa mmalo, adali ndi akazi 70.

Related Posts

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

 I am hated in Malawi – Zuneth Sattar

 I am hated in Malawi – Zuneth Sattar

British business tycoon Zuneth Sattar who faces accusations of alleged corruption has said he is the most hated person in Read more

The British NCA Operations In Malawi Remain Questionable, Britons Aim To Topple Tonse Government

Exposed! British NCA bankrolls PIJ to victimize successful business persons, politicians, judges in Malawi The truth be told! The establishment Read more

President Chakwera arrives in Namibia for funeral ceremony of late Hage Geingob

Windhoek, February 24: President Dr Lazarus Chakwera has touched down in Windhoek, Namibia, to join the nation in bidding farewell Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window