Fri. Apr 26th, 2024

Nkhani Za Fertilizer Ku Dowa Central East

By Rev. Flywell Somanje.

Malinga ndikafuku yemwe wachitika ndi Bungwe la MiRECE, mosemunja yambikira tchito yongawa fertilizer Dziko Muno athu odzungulira Dowa Boma sanapezebe fertilizer mpaka lero, chikuyimitsa mutu athu ndi chakuti apa ndi pa mchombo pa Boma la Dowa, Koma fertilizer akungawidwa kwambiri kumandera komwe ma MP akuchokera, ku Mvera komwe akuchokera MP chimwendo, KU dera la Lumbadzi komwe akuchokera MP DAUD,ku Chibazi konwe akuchokera MP Kawale zikuyendaso, fuso ndikumati athu aku Dowa Central east analakwanji, madadaulo awo achuluka, KU derari palibe chitukuko cholozeka chosecho ma MP atatu onse amathera pamenepa, m’mbuyomu Bungwe lanthu (MIRECE) linapempa kuti MEC idure dera, (consutuency) Tikuthoza MEC kuti zinachika, Koma izi sizikutathauza kuti ma MP atatuwa aleke kugwira tchito KU derari palipano Monga zikukhalilamu, iwompaka 2025 akadzachita masakho! Tikupepha Bungwe la MEC kuti naloso liunikire’ Sibwino kuti Zika Zina zizimanidwa chitukuko Dziko lomwelino! Rev somanje!

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open