Kutsatira mvula yochuluka imene inadza kamba ka Namondwe wa Freddy, nyanja ya Chilwa ku Zomba yadzadza pomwe madzi tsopano afika midzi yoyandikana ndi nyanjayi.
Malingana ndi a Fanuel Sadik, amene amakhala kuderali, madzi afika midzi yoyandikila doko la Kachulu komanso Mchenga ndipo anthu asamukira madera ena.
Khansala waderali, a Douglas January, anatsimikiza izi ndipo anati pakali pano kufika kunyanjaku pagalimoto ndikosatheka.
Zithuzi zikuonetsa momwe zinthu ziliri ku nyanjayi.
MALAWI
FREEDOM
NETWORK
United for Freedom, Justice and a Better Malawi
Airtel Money
0994095804
Mpamba
0881428759
FDH Bank
Acc No:
1400000670385NBS Bank
Acc No:
10118988Thank you for your support!