Nduna yowona za chitetezo cha mdziko, Ken Zikhale Ng’oma yalandira mendulo ya ulemu kamba ka ntchito yomwe akugwira pogwira ndi kutumiza ku Rwanda anthu omwe akuganiziridwa kuti anapalamula milandu yokhuza nkhondo.

Malinga ndi Ng’oma, anthuwa akhala akufunidwa kuyambira mchaka cha 1994 ndipo boma likusaka anthu ena asanu kuti nawo atumizidwe ku Rwanda.

Malinga ndi Ng’oma, mphotoyi apereka ndi akulu akulu a dziko la Rwanda.

Dziko la Rwanda linalengeza kuti yemwe azapeze anthuwa azalandira chionamaso cha ndalama zokwana 2.5 million zamdziko la Amerika zomwe ndi pafupi fupi 2.5 billion kwacha.

Lachitatu lino anthu ena okwana makumi anayi akuyembekezeka kutumizidwanso ku Rwanda.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *