By Comrade jumbe
Pa chichewa pali mawu amatero kuti tsogolo ndi la iwo amene akukonzekera lero ,
Abale ndi alongo lero ndi mwayi wina wofunikira kwambiri kwa nzika iliyonse yomwe ikufunira zanwino dziko lino .
Mmene kalembera wa zisankho afika ku mapeto uwu ndi mwayi wathu womaliza wokonzekera kusintha komwe tonse amalawi takhala tikuyembekezera.
Chisankho chomwe chikubwerachi sichinthu chongochitika mwachizoloŵezi monga mwa nthawi zonse koma ndi nthawi yofunika kwambiri m’mbiri ya dziko lathu.
Kukhala chete osatenga nawo gawo liri lonse pa chisanko pamene ena akusankha tsogolo lathu ndi kuzimpwanyila tokha ufulu okonza tsogolo la dziko lathu chifukwa mphamvu zobweretsa kusintha zili mu voti yathu ndipo uwu ndi mwayi wotsiriza popeza kulembetsa kwa mec kwafika kumalecheleche.
Tiyenela kukumbukira kuti mtsinje umadzadza ndi dontho limozi limozi kulembetsa kwanu kungawoneke ngati kochepa koma kukalumikizana ndi mamiliyoni ena kumakhala mphamvu yomwe palibe munthu olo boma linganyalanyaze.
Ndikumema inu nonse amalawi kuti pitani mukalembetse mukawundula wazisankho auzeni anzanu akubanja lanu ndi aneba kuti achitenso chimodzimodzi.uwu ndi mwayi wathu kuti tichotse omwe alephera ndikusankha atsogoleri omwe adzayike miyoyo ya anthu patsogolo.
Chisankho cha mu September sichisankho chabe chifukwa amalawi talira kokwana ndipo tikulira kotero ndi nthawi yathu yobweretsa kusintha komwe takhala tikudikirira.
Kalembetseni lero ndikuteteza liwu lanu pokonza tsogolo la dziko lathu. mphamvu ili m’manja mwathu tiyeni tigwiritseni ntchito mwanzeru .
pamodzi tingathe
- Museveni under fire: “If You Can’t Afford Fuel, Stay Home” — Remarks Spark Outrage Across Uganda
- Kalindo thanks government for accepting fuel crisis in Malawi
- MHRRC supports media tour on service delivery gaps in Dowa
- Press Cane completes K10 billion waste to fertilizer plant
- Why Lazarus Chakwera Skipped the Amaryllis Hotel Inquiry — And Why the Report Remains Incomplete
- Ansah to Spearhead Malawi’s Economic Revival
- NBS Bank finances Lindian US$11.6M equipment
- Breaking News: Fuel Price Increase Temporary, Says Analyst Suleman Chitera
- Nkhani Yachilengedwe: Kukwera kwa Mitengo ya Mafuta ndi Kwakanthawi – Akutero Wofufuza Suleman Chitera
- Fuel Price Increase in Malawi Linked to Iran–US War Global Oil Crisis, Not Domestic Policy –Suleman Chitera
- BMTV calls police to arrest Chakwera for issuance of passport to a foreigner
- NBM plc appoints Bernard Masi as Head of Corporate Banking Division
- Atupele Muluzi Urges Urgent Economic Reforms as Malawi Faces Deepening Crisis
- Malawi Fuel Shortage Update: Government Assures 7 Days Fuel Stock as Supply Stabilises
- Malawi Fuel Crisis: Why DPP’s Transparency and Economic Recovery Efforts Deserve Public Patience
- Chitera says Mutharika is leading Malawi from “Bagamoyo” to “Canaan”
- World Bank Rapid Response Facility to Support Malawi Economy Amid Global Crisis
- Hungary PM Péter Magyar Says Country Will Enforce ICC Arrest Warrant on Benjamin Netanyahu

















