By Comrade jumbe
Pa chichewa pali mawu amatero kuti tsogolo ndi la iwo amene akukonzekera lero ,
Abale ndi alongo lero ndi mwayi wina wofunikira kwambiri kwa nzika iliyonse yomwe ikufunira zanwino dziko lino .
Mmene kalembera wa zisankho afika ku mapeto uwu ndi mwayi wathu womaliza wokonzekera kusintha komwe tonse amalawi takhala tikuyembekezera.
Chisankho chomwe chikubwerachi sichinthu chongochitika mwachizoloŵezi monga mwa nthawi zonse koma ndi nthawi yofunika kwambiri m’mbiri ya dziko lathu.
Kukhala chete osatenga nawo gawo liri lonse pa chisanko pamene ena akusankha tsogolo lathu ndi kuzimpwanyila tokha ufulu okonza tsogolo la dziko lathu chifukwa mphamvu zobweretsa kusintha zili mu voti yathu ndipo uwu ndi mwayi wotsiriza popeza kulembetsa kwa mec kwafika kumalecheleche.
Tiyenela kukumbukira kuti mtsinje umadzadza ndi dontho limozi limozi kulembetsa kwanu kungawoneke ngati kochepa koma kukalumikizana ndi mamiliyoni ena kumakhala mphamvu yomwe palibe munthu olo boma linganyalanyaze.
Ndikumema inu nonse amalawi kuti pitani mukalembetse mukawundula wazisankho auzeni anzanu akubanja lanu ndi aneba kuti achitenso chimodzimodzi.uwu ndi mwayi wathu kuti tichotse omwe alephera ndikusankha atsogoleri omwe adzayike miyoyo ya anthu patsogolo.
Chisankho cha mu September sichisankho chabe chifukwa amalawi talira kokwana ndipo tikulira kotero ndi nthawi yathu yobweretsa kusintha komwe takhala tikudikirira.
Kalembetseni lero ndikuteteza liwu lanu pokonza tsogolo la dziko lathu. mphamvu ili m’manja mwathu tiyeni tigwiritseni ntchito mwanzeru .
pamodzi tingathe
- Kalindo crowns Mutharika statesman for rejecting CDF Bill signing
- Mhango Orders Crackdown on Driving Schools as Road Deaths Spiral
- Politics of entitlement: MCP’s cyclophony of self-serve
- Controversy Erupts Over US-South Africa Refugee Deal
- Public Demands Accountability: Why Chimwendo Banda’s Case Must Set a National Precedent
- Walter Nyamilandu Manda Leads Community-Centered Flood Response in Nsanje
- A Dangerous Game at Sea: Putin, Trump, and the Rising Specter of Global Confrontation
- Mutharika sides with Malawians withholding consent to CDF
- Kabambe Calls for United National Action as UTM Extends Lifeline to Flood Victims in Dwangwa
- Kamphangala accuses MCP members of calling for Chimwendo’s release
- Malawi at A crossroads: The K21 Trillion question that demands answers
- China Unveils Next-Generation Strategic Missile Launcher with Breakthrough Mobility
- 2026 Audi Q3 Unveiled: Quattro All-Wheel Drive, Premium Interior and Advanced Digital Tech
- Why is Malawian Sugar cheaper in Zambia than at home?
- Mutharika Blocks CDF Amendment, Citing Weak Oversight and Risk of Abuse
- Print & Cut Steps Forward to Restore Iconic Mangochi Sign
- Malawi, Egypt Deepen Strategic Ties as Investment and Cooperation Agenda Expands
- Is the Vice President of Malawi Supposed to Use Public Resources for Private Life Affairs? A Litmus Test for “Return to Proven Leadership”



















