
“Tikuzunzika Tipatseni Malipiro Athu
Anthu ena ogwira ntchito ku bungwe la ADMARC adandaula kuti akuzunzika komanso kuponderezedwa kuchokera pomwe boma lidatseka bungweli kuti likonze zinthu.
Izi azinena pomwe anthu oposa 300 ogwira ntchito ku bungweli achita zionetsero m’mawawu pofuna kukamiza boma kuti liwapatse malipiro awo a mwezi wa September ndi October.
Iwo akufunanso boma lichite machawi pokonzanso zinthu ku bungweli.
Read also: Tobacco sales sees suspension on the opening day
Read also: MDF To Conduct Live Firing Training Exercise In Chikala Hills
Read also: Kalua feels sorry with the passing of electoral amendment bill
Ambiri mwa omwe amachita zionetserozi anavala makaka akuda.
Anthu okwana 4687 akuyembekezeka kuchotsedwa ntchito ku ADMARC pomwe boma likuti likufuna kukonzanso ntchito za bungweli pomwe zikumveka kuti ogwira ntchito ena amasaka chuma.
Read also: Fugitive Zambian MP arrested in Zimbabwe – minister
Read also: RBM unveils new K10,000 banknote: A step towards efficient currency management
Read also: Women Urged to Lead in Socioeconomic Growth



















