Malawi Freedom Network
Giving you daily news that rock the world

Salima Sec ikubwera ndi K 150 million kuchokera ku South Africa

Timu ya Salima Secondary School yamalizira pa nambala yachitatu mu mpikisano wa African Schools Championship kutsatira kugonjetsa timu ya Sainte Rita 3-1

Blessings Sakala, Ishmael Bwanali komanso Latumbikika Kayira ndi omwe anagoletsa kumbali ya Salima Secondary school

Salima secondary school itenga ndalama zokwana $150,000 (pafupifupi K150 milllion) pomaliza pa nambala yachitatu

Leave a Comment

Leave a review

This website uses cookies to improve your experience. We'll assume you're ok with this, but you can opt-out if you wish. Accept Read More