Akatswiri adzudzula boma la mgwirizano wa Tonse ati kamba kosakwaniritsa ena mwa malonjeza omwe unapereka kwa a Malawi usanalowe m’boma.
Izi zikubwera pomwe patha zaka zitatu dziko lino litachititsa chisankho chamtsogoleri chachibweleza pa 23 June mchaka cha 2020.
Moses Mkandawire, Wapampando wa bungwe la National Anti-Corruption Alliance, wati pakhala pali nkhani zakatangale zokhudza akuluakulu ena aboma.
Read also: MEC announces preliminary voter registration figures for 2025 General Election
Read also: BMTV says No Black box no final report on SKCs death
Read also: Chigamula urges community leaders to support him ahead of general elections
Mkandawire wati izi ndi chifukwa choti bomali silikuikila chidwi chenicheni chithana ndi mchitidwe wa katangale.
Mkuikilapo ndemanga yake George Phiri katswiri pa nkhani za ndale wati kulephela kwa boma la mgwilizano wa Tonse kukwanilitsa zomwe linalonjeza kukukwiitsa amalawi
Read also: ACB wins against Batatawala, others
Read also: Kalindo advises politicians not to take citizens for granted
Read also: Govt To Provide Adequate Investiment In Digitilisation





