Akatswiri adzudzula boma la mgwirizano wa Tonse ati kamba kosakwaniritsa ena mwa malonjeza omwe unapereka kwa a Malawi usanalowe m’boma.

Izi zikubwera pomwe patha zaka zitatu dziko lino litachititsa chisankho chamtsogoleri chachibweleza pa 23 June mchaka cha 2020.

Moses Mkandawire, Wapampando wa bungwe la National Anti-Corruption Alliance, wati pakhala pali nkhani zakatangale zokhudza akuluakulu ena aboma.

Mkandawire wati izi ndi chifukwa choti bomali silikuikila chidwi chenicheni chithana ndi mchitidwe wa katangale.

Mkuikilapo ndemanga yake George Phiri katswiri pa nkhani za ndale wati kulephela kwa boma la mgwilizano wa Tonse kukwanilitsa zomwe linalonjeza kukukwiitsa amalawi

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *