Akatswiri adzudzula boma la mgwirizano wa Tonse ati kamba kosakwaniritsa ena mwa malonjeza omwe unapereka kwa a Malawi usanalowe m’boma.
Izi zikubwera pomwe patha zaka zitatu dziko lino litachititsa chisankho chamtsogoleri chachibweleza pa 23 June mchaka cha 2020.
Moses Mkandawire, Wapampando wa bungwe la National Anti-Corruption Alliance, wati pakhala pali nkhani zakatangale zokhudza akuluakulu ena aboma.
Read also: Kalindo says Malawians should expect no arrest from Amaryllis Hotel sale
Read also: Dowa South East Parliamentarian Launches Construction Of Chunzu CDSS
Read also: MAU impressed with junior swimmers performance
Mkandawire wati izi ndi chifukwa choti bomali silikuikila chidwi chenicheni chithana ndi mchitidwe wa katangale.
Mkuikilapo ndemanga yake George Phiri katswiri pa nkhani za ndale wati kulephela kwa boma la mgwilizano wa Tonse kukwanilitsa zomwe linalonjeza kukukwiitsa amalawi
Read also: New Mobile Service Provider Company Malcel Rolls Out
Read also: Hope For Improved Efficiency As Maneb Launches E-System
Read also: Manaf Launches Sign Language Dictionary





