Nyumba Ya Malamulo Yakambirana Za Chamba

Aphungu akambirana ndi kuvomereza kuti pakhale lamulo loloreza dziko lino kumalima fodya wa mkulu wa chamba.

Aphunguwa avomerezana kuti kulima mbewuyi kuthandiza kuti dziko lino lidzipeza ndalama zochuluka.

Phungu wa ku m’mwera kwa Lilongwe a Peter Dimba ndi omwe anabweretsa nkhaniyi m’nyumbayi.

Kwa nthawi yaitali pakhala pali lingaliro loloreza ulimi wa chamba-wu omwe ambiri akhala akunena kuti uli ndi kuthekera kotengera chuma cha dziko lino patsogolo.

Asanakambirane nkuvomerezana izi aphunguwa , kupezeka ukulima mbewuyi umakhala mlandu omwe anthu ambiri akugwira nawo jele m’ndende zosiyanasiyana m’dziko muno.

Related Posts

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

The Concerned Citizens Furious With Chizuma’s Stubbornness

The concerned citizens group which is advocating for sanity in civil service have vowed to take drastic measures in responding Read more

Mirece supports land reclamation bought by foreigners

Reverend Flywell Somanje…. this is the way to go A governance and human rights organization, the Millennium Information and Resource Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window