Sat. Apr 27th, 2024

Nyumba Ya Malamulo Yakambirana Za Chamba

Aphungu akambirana ndi kuvomereza kuti pakhale lamulo loloreza dziko lino kumalima fodya wa mkulu wa chamba.

Aphunguwa avomerezana kuti kulima mbewuyi kuthandiza kuti dziko lino lidzipeza ndalama zochuluka.

Phungu wa ku m’mwera kwa Lilongwe a Peter Dimba ndi omwe anabweretsa nkhaniyi m’nyumbayi.

Kwa nthawi yaitali pakhala pali lingaliro loloreza ulimi wa chamba-wu omwe ambiri akhala akunena kuti uli ndi kuthekera kotengera chuma cha dziko lino patsogolo.

Asanakambirane nkuvomerezana izi aphunguwa , kupezeka ukulima mbewuyi umakhala mlandu omwe anthu ambiri akugwira nawo jele m’ndende zosiyanasiyana m’dziko muno.

Related Posts
NRWB Secures 47 million Euros (K90 billion) from European Investment Bank

Northern Region Water Board (NRWB) has secured about 47 million Euros (K90 billion) from European Investment Bank (EIB), to be Read more

Kapito trashes Illovo Sugar’s assertions on sugar scarcity

Consumers Association of Malawi (CAMA) Executive Director, John Kapito, has described Illovo Sugar’s assertions on reasons of the commodity’s scarcity Read more

Dowa Nice Trust assures CSO network on good coordination

By Vincent Gunde District Civic Education Expert for Nice Trust in Dowa Alinafe Chikakuda, says Nice Trust is committed to Read more

88 Percent Population Access Clean Safe Water

About 88 percent of the country’s population now has access to clean and safe water. The revelation comes alongside the Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open