Mitawa Ayima Opanda Opikisana Naye

Ogwilizira mpando wa mtsogoleri wa bungwe la Super League of Malawi(Sulom), Colonel Gilbert Mitawa ayimira pa mpando wa mtsogoleri wa bungweri opanda opikitsana nawo.

Izi zikutsatira chikalata chomwe atulutsa a Crowe Howarth Malawi omwe amayendetsa ndondomeko yolandila ma kalata a anthu ofuna kuzayimila pa maudindo ku bungwe la Sulom omwe anatseka kulandila ma kalatawa.

A Mitawa omwe amagwilizira udindo’wu kutsatira kwa kuchoka kwa Fleetwood Haiya amene pano ndi mtsogoleri wa bungwe la Football Association of Malawi akuyembekezeka kupitiliza ngodya zomwe anasiya a Haiya zofuna kusintha mpira.

Pa udindo wa mamembala a komiti yayikulu ya bungweri pali anthu atatu omwe akupikisana omwe ali Isaac Mdindo, William Nhlane ndi Charles Manyungwa.

Zisankho zizachitika pa 30 March, 2024 mu mzinda wa Lilongwe.

Related Posts

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

The Concerned Citizens Furious With Chizuma’s Stubbornness

The concerned citizens group which is advocating for sanity in civil service have vowed to take drastic measures in responding Read more

Zuneth Sattar Speaks Out- I’m Not Shaken, It’s Just Mere Social Media Speculations

Public is being fed with social media lies propagated by some misguided individuals over personal vendetta. The move is just Read more

The British NCA Operations In Malawi Remain Questionable, Britons Aim To Topple Tonse Government

Exposed! British NCA bankrolls PIJ to victimize successful business persons, politicians, judges in Malawi The truth be told! The establishment Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window