Lipipa Amanga Chipatala Cha Manase

Ichi ndi chipatala cha Manase chomwe akumanga ndi Phungu wa Blantyre City South wolemekezeka a Noel Lipipa.

Kubwera kwa a Noel Lipipa ku dera la Blantyre City South zinthu zambiri zikuchitika ndipo zitukuko ndie ndi mbwee.

Anthu aku derali ayamikira a Lipipa kamba kogwiritsa ntchito Constituency Development Fund (CDF) moyenerera.

Noel Lipipa kusintha Blantyre City south!

Related Posts

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

AGHF Feeds Patients, Guardians At Mangochi District Hospital

A giving hand foundation is a local organisation working in various programs in Malawi. On Thursday the organization together with Read more

Kalindo Wapempha Chakwera Achotse Ntchito Chizuma Masiku Okwana Asanu Ndi Awiri

Mkulu wa bungwe la Concerned Citizens and Timely Voices (CCTV) Bon Kalindo, wapempha mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera Read more

The Concerned Citizens Furious With Chizuma’s Stubbornness

The concerned citizens group which is advocating for sanity in civil service have vowed to take drastic measures in responding Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window