Ichi ndi chipatala cha Manase chomwe akumanga ndi Phungu wa Blantyre City South wolemekezeka a Noel Lipipa.
Kubwera kwa a Noel Lipipa ku dera la Blantyre City South zinthu zambiri zikuchitika ndipo zitukuko ndie ndi mbwee.
Anthu aku derali ayamikira a Lipipa kamba kogwiritsa ntchito Constituency Development Fund (CDF) moyenerera.
Noel Lipipa kusintha Blantyre City south!