By Comrade jumbe
Pa chichewa pali mawu amatero kuti tsogolo ndi la iwo amene akukonzekera lero ,
Abale ndi alongo lero ndi mwayi wina wofunikira kwambiri kwa nzika iliyonse yomwe ikufunira zanwino dziko lino .
Mmene kalembera wa zisankho afika ku mapeto uwu ndi mwayi wathu womaliza wokonzekera kusintha komwe tonse amalawi takhala tikuyembekezera.
Chisankho chomwe chikubwerachi sichinthu chongochitika mwachizoloŵezi monga mwa nthawi zonse koma ndi nthawi yofunika kwambiri m’mbiri ya dziko lathu.
Kukhala chete osatenga nawo gawo liri lonse pa chisanko pamene ena akusankha tsogolo lathu ndi kuzimpwanyila tokha ufulu okonza tsogolo la dziko lathu chifukwa mphamvu zobweretsa kusintha zili mu voti yathu ndipo uwu ndi mwayi wotsiriza popeza kulembetsa kwa mec kwafika kumalecheleche.
Tiyenela kukumbukira kuti mtsinje umadzadza ndi dontho limozi limozi kulembetsa kwanu kungawoneke ngati kochepa koma kukalumikizana ndi mamiliyoni ena kumakhala mphamvu yomwe palibe munthu olo boma linganyalanyaze.
Ndikumema inu nonse amalawi kuti pitani mukalembetse mukawundula wazisankho auzeni anzanu akubanja lanu ndi aneba kuti achitenso chimodzimodzi.uwu ndi mwayi wathu kuti tichotse omwe alephera ndikusankha atsogoleri omwe adzayike miyoyo ya anthu patsogolo.
Chisankho cha mu September sichisankho chabe chifukwa amalawi talira kokwana ndipo tikulira kotero ndi nthawi yathu yobweretsa kusintha komwe takhala tikudikirira.
Kalembetseni lero ndikuteteza liwu lanu pokonza tsogolo la dziko lathu. mphamvu ili m’manja mwathu tiyeni tigwiritseni ntchito mwanzeru .
pamodzi tingathe
- SULOM Fines Nyasa Big Bullets K3.35 Million Over Match-Day Misconduct
- CFAO Mobility Malawi Unveils Nine New 2026 Toyota Hilux Ranges
- Asilamu ndi Ayawo Apereka Chenjezo: “Musatigwiritse Ntchito Pa Mavoti Koma Kutisiyira Mbali Mukagawana Mphamvu”
- Muslims and Yaos Push Back: “Stop Using Us for Votes While Sidelining Us in Government”
- Airtel Malawi Awards Nzeru Tech Scholarships to 25 MUST Students
- Silver Strikers Ladies’ Historic CAF Champions League Journey Ends in Narrow Defeat
- Father vs Son: Mpinganjiras Set for Emotional Airtel Top 8 Final Showdown
- NBM plc donates K10 million to IMM lake conference
- Kasungu chiefs decry ESCOM transformer vandalism
- Press Cane starts organic fertiliser production
- Rhodrick Junaid Kalumpha Steps Up to Restore Cooking at Mangochi District Hospital
- CCM-PPM Demands NOCMA Board Dissolution Over K700 Million Transfer
- Let Us Be Honest With One Another: Malawi Was Blessed With APM
- 22nd Agriculture Fair Opens in Blantyre as Malawi Pushes Agricultural Transformation
- Study Raises Concerns Over Political Representation of Muslims and Yaos in MCP and DPP Governments
- Kafukufuku Wadzudzula MCP ndi DPP pa Kugwiritsa Ntchito Asilamu ndi Ayao pa Ndale
- NOCMA K700 Million Fuel Payment Dispute Raises Questions as NAPP Demands Answers
- NOCMA Deputy CEO Micklas Reuben Arrested Over Alleged $403,615 Fuel Transaction
Read also: Eight-year-old girl and 34-year-old man seriously injured in West London shooting, Met Police says
Read also: Wealth Accumulation Among MCP Former Cabinet Ministers Raises Public Eyebrows
Read also: Malawi To Have State of Art Private Cancer Centre In Blantyre












