Sat. Apr 20th, 2024

Anthu ochita ziwonetsero ati a Chakwera atule pansi udindo

Anthu okhudzidwa omwe akudana ndikukwera kwa mitengo ya zinthu mumzinda wa Blantyre ati apempha mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera kuti atule pansi udindo wawo kamba kolephera kusintha dziko lino monga momwe analonjezera.

Onthuwa anatsogoleredwa ndi Oliver Nakoma.

Anthuwa adayamba kuyenda kuchokera ku Roundabout ku Limbe kudzera ku Masauko Chipembere Highway kupita ku ofesi ya mkulu wa boma ku Blantyre.

Ndipo chitetezo chinali chokhwima chifukwa kunali apolisi ambiri. “`

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation