Anthu okhudzidwa omwe akudana ndikukwera kwa mitengo ya zinthu mumzinda wa Blantyre ati apempha mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera kuti atule pansi udindo wawo kamba kolephera kusintha dziko lino monga momwe analonjezera.
Onthuwa anatsogoleredwa ndi Oliver Nakoma.
Anthuwa adayamba kuyenda kuchokera ku Roundabout ku Limbe kudzera ku Masauko Chipembere Highway kupita ku ofesi ya mkulu wa boma ku Blantyre.
Ndipo chitetezo chinali chokhwima chifukwa kunali apolisi ambiri. “`
Read also: Eradicating polio would eradicate so much tragedy
Read also: Malawi at A crossroads: The K21 Trillion question that demands answers
Read also: THE IMF’S CLIMATE CHANGE DEBATE

