Boma Laitanitsa Ogwira Ntchito 1000 Ku Admarc

Boma laitanitsa ogwira ntchito ku ADMARC okwana 1000 kuti athandizire kugawa zipangizo za ulimi zotsika mtengo mu ndondomeko ya AIP.

Nduna yaza ulimi, Sam Kawale yatsimikiza izi dzulo ku nyumba ya malamulo.

M’mbuyomu, nduna yakale yaza ulimi, Lobin Lowe idayamba yaimitsa anthu onse ogwira ntchito ku ADMARC ati pofunanso kukonza ntchito za bungweli.

Kodi chiganizo choitanitsa anthuwa boma lisadamalize kukonzanso ADMARC nkolondola?

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window