Boma laitanitsa ogwira ntchito ku ADMARC okwana 1000 kuti athandizire kugawa zipangizo za ulimi zotsika mtengo mu ndondomeko ya AIP.
Nduna yaza ulimi, Sam Kawale yatsimikiza izi dzulo ku nyumba ya malamulo.
M’mbuyomu, nduna yakale yaza ulimi, Lobin Lowe idayamba yaimitsa anthu onse ogwira ntchito ku ADMARC ati pofunanso kukonza ntchito za bungweli.
Kodi chiganizo choitanitsa anthuwa boma lisadamalize kukonzanso ADMARC nkolondola?
Read also: Buluma Expose Fuel Dirty Deals At Nocma, Implicates MCP Top Politicians
Read also: CDEDI Questions Legality of Cabinet Meeting, Demands Answers from Government
Read also: What if Atupele Muluzi has a political message for Malawians?

