Khansara wa MCP a Gabriel Mwaungulu atula pansi udindo wawo

Khansala wa chipani cha Malawi Congress Party (MCP) wa Ward ya Chibavi East a Gabriel Mwaungulu atula pansi udindo wawo ndipo walowa chipani cha Alliance for Democracy (AFORD).

Mwaungulu adalengeza kusiya ntchito yake Lamulungu pa msonkhano wokumbukira zaka 30 womwe a Enoch Chihana adakonza pa Chibavi Ground mumzinda wa Mzuzu.

Khansala walonjeza kuti agwira ntchito molimbika pokopa anthu kuti avotere Chihana ndi AFORD pa chisankho chomwe chikubwera cha 2025.

Panopa bungwe la AFORD likuchita misonkhano m’dziko muno zisankho zisanachitike.

Chipanichi chikuyembekezeka kuchita msonkhano wawo wachisankho mu Seputembala

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window