Mbilizi ndi anzake atuluka pa belo

Views: 1
0 0

Read Time:24 Second

Bwalo la magistrate ku Blantyre latulutsa pa belo yemwe anali wachiwiri kwa komishonala wa bungwe lotolela msonkho la MRA a Roza Mbilizi ndi anzawo ena awiri

Anthuwa anawamanga kaamba kowaganizira kuti adagwiritsa ntchito molakwika nambala yopelekera msonkho (TPIN) ya mtsogoleli wakale wa dziko lino a Peter Mutharika.

Bwaloli lalamula atatuwa kuti alipile K 350,000 ngati chikole komanso kuti apeleke ku bwaloli zikalata zawo zoyendera komanso anthuwa auzidwa kuti azikaonekera ku mafesi a ACB pa sabata ziwiri zili zonse

Happy

Happy

0 %

Sad

Sad
0 %

Excited

Excited
0 %

Sleepy

Sleepy

0 %

Angry

Angry
0 %

Surprise

Surprise
0 %

Average Rating

5 Star
0%
4 Star
0%
3 Star
0%
2 Star
0%
1 Star
0%

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *