Friday, March 29
Shadow

Sitikupanga Nawo Ena Alandira K60 Million

Gulu lina lomwe likudzitcha kuti Civil Society for Unity of Purpose ladzambatuka ku Lilongwe komwe likuti silitenga nawo gawo pazionetsero za mawa ponena kuti omwe akonza zionetserozi alandira ndalama ku zipani zotsuta.

M’neneri wa gululi, Agape Khombe, yemwe m’mbuyomu adali ku gulu la Mbadwa Zokhudzidwa, akuti omwe akutsogolera zionetserozi alandira K60 million.

Koma Khombe analephera kupereka umboni kwa olemba nkhani pa nkhani-yi ngakhale anati anthu ena masiku ano akugwiritsa ntchito zionetserozi pofuna kupeza zofuna zawo.

Koma omwe akonza zionetserozi zadayankhepo pa izi.

Mwa zina, zionetsero za mawa ku Lilongwe zikufuna kukapereka madando kwa President Lazarus Chakwera ku nyumba ya chifumu pa mavuto omwe akuta dziko lino kuphatikizapo katangale.

Gulu la Action Against Impunity ndi lomwe likutsogolera zionetserozi.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation