Wednesday, September 27Malawi's top news source
Shadow

Tag: Vera Kamtukule

MCP General Membership Idabwa Ndi Ulamuliro Wa Chakwera

MCP General Membership Idabwa Ndi Ulamuliro Wa Chakwera

Politics
Mchithunzi, Kantukule kulandira President Chakwera pa Kamuzu International Airport}. Gulu lomwe likudzitchula kuti General Membership of Malawi Congress Party laonetsa kudabwa kuti President Lazarus Chakwera adasankha nduna yaza ntchito Vera Kantukule kuyang’anira dziko pomwe ankapita ku Mozambique m’mwezi wa April chaka chino chikhalirecho ndunayi siya MCP komanso ilibe udindo ulionse mchipanichi. Iwo akuti a Chakwera akanatha kusankha amai ena mchipanichi omwenso ali nkuthekera pomwe ati pa ndale mtsogoleriyu adaphonya. Izi ndi malinga ndi kalata yomwe gululi latulutsa pomwe latinso anthu ochulula omwe analembedwa ntchito ku nyumba ya boma {State House} ndi a mpingo wa Assemblies of God. Kalatayi yomwe yasainidwa ndi m’neneri wake, Zinenani Magola komanso wapampando, Alex M...
Police Arrested 51-year-old Dauka Manondo For insulting Minister of Labour Vera Kamtukule On social media post.

Police Arrested 51-year-old Dauka Manondo For insulting Minister of Labour Vera Kamtukule On social media post.

Local
Police in Lilongwe have arrested 51-year-old Dauka Manondo on allegations that he insulted Minister of Labour Vera Kamtukule in a social media post. Lilongwe Police Public Relations Officer Hastings Chigalu has confirmed the arrest. According to Chigalu, Manondo posted a picture of the minister taken at Kamuzu International Airport, on a WhatsApp group called ‘Our political square’, and captioned it with insulting words. The picture is said to have been taken at the airport when President Lazarus Chakwera was returning from Mozambique. Kamtukule led the team of officials who welcomed the President.