Fri. Apr 26th, 2024

KAZAKO Awopseza Kutsegula Makampani Ophika Mafuta Ngati Mitengo satsitsa

By ADMIN Mar15,2022

Minister of Information Gospel Kazako yawopseza makampani opanga mafuta ophikira kuti boma likhoza kuyambitsa kampani yake yopanga mafuta ngati mitengo sitsika.

A Kazako anena izi pokambirana ndi atolankhani a boma mu mzinda wa Lilongwe.

Malinga ndi a Kazako n’zachisoni kuti mitengo ya mafuta ophikira ikukwerabe ngakhale boma likuchitapo kanthu pa madandaulo awo a msonkho.

Mwezi watha, Nduna ya Zachuma Sosten Gwengwe adalengeza za kuchotsa msonkho wa Value Added Tax (VAT) pamafuta ophikira ndi zinthu zina.

Amalawi ankayembekezera kuti mitengo ya mafuta idzatsika mwatsoka, mitengo ikukwerabe.“`

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

By ADMIN

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open