NDIKUFUNA NANKHUMWA AZIMUGWADIRA MUTHARIKA-Namalomba

IMG 20220315 092008

Mneneri wa Chipani cha DPP a Shadreck Namalomba,awunza Kondwani Nankhumwa kuti asamapange ziganizo payekha akafuna kuchita zinthu.

A Namalomba ati,Nankhumwa akamafuna kuchita chinthu chokhuzana ndi mu chipani cha DPP, aziyamba amufusa kale mtsogoleri wa Chipanichi a Mutharika kamba koti iye ndi wamkulu.

Namalomba amalankhula izi ku mkumano womwe udaliko dzulo ku Mangochi.

A Namalomba ,awunza anthu kuti a Nankhumwa ndi munthu wotsokoneza mu chipani ndipo Peter Mutharika,ndiwokhumudwa ndi zomwe Nankhumwa akuchita.“`

0 0 votes
Article Rating
Subscribe
Notify of
guest
0 Comments
Oldest
Newest Most Voted
Inline Feedbacks
View all comments
//otieu.com/4/9370459
0
Would love your thoughts, please comment.x
()
x