a Msaka ati ngati iwo adzasankhidwe kukhala mtsogoleli wa chipani cha DPP mchaka cha 2023, maso awo adzakhala kudzapambana pa chisankho cha utsogoleli wa dziko cha mchaka cha 2025.
Iwo ati ali ndi khumbo lobwezeretsa umodzi mchipani cha DPP akawina pa mpandowu.
Read also: Labour Minister Demands Better Pay and Conditions for Kaziwiziwi Coal Mine Workers
Read also: Malawi Senior Men’s Cricket Team Wins Silver at ICC T20 World Cup Sub-Regional Africa Qualifiers
Read also: DPP Gears Up to Rebuild What Chakwera and MCP Destroyed
Iwo atinso cholinga chawo ndikudza konzanso chuma cha dziko lino chomwe ati chasokonekera pakanali pano.
“Ichi ndichiyambi cha Malawi wokonzeka” Msaka.
Read also: Chakwera Inaugulates Macoha Flag Week
Read also: Let Justice Flow Like a River: A Call for Electoral Transparency and Accountability
Read also: Self Help Africa to implement demand-side subsidies project





