Yemwe amayankhulira mgwirizano wa Tonse, Kamuzu Chibambo wati mafuta a galimoto omwe nduna komanso alembi m’boma amalandira atsike kuchoka pa 2000 liters kufika pa mulingo osapyola 750 liters pamwezi ngati njira imodzi yotetezera chuma chadziko lino.
Chibambo, yemwenso ndi mtsogoleri wa chipani cha Peoples Transformation-PETRA walankhula izi pa msonkhano wa olemba nkhani munzinda wa Blantyre.
Read also: Peter Mutharika Leads 2025 Presidential Race with Significant Youth Support, New Survey Shows
Read also: Kaweche promises transparency, accountability, and community empowerment
Read also: Chigamula urges community leaders to support him ahead of general elections
Iye watsindika kufunika kokhazikitsa kapena kutsatira mfundo zotukulira chuma kuti dziko lino lidzitha kukhala ndi ndalama zothetsera vuto lakusowa kwa ndalama zakunja.
Atakumana atsogoleri a Tonse miyezi yapitayo, Chibambo adauza a Malawi kuti adakambirana mfundo zothetsera mavuto a chuma omwe ayala mphasa m’dziko lino pakadalipano.
Read also: Onjezani Kenani critiques Malawi’s judicial system on social media
Read also: Anti Martha Chizuma demonstrations On Monday
Read also: Chiutsi dumps PDP, to reunite with DPP





