Mkulu wa malamulo m’dziko muno Thabo Chakaka Nyirenda ali m’dziko la Germany kusaka ndalama za amerika zokwana 543,000 zomwe zidasowa pomwe boma limafuna kugula feteleza
Chakaka Nyirenda wati ali kumeneko kulondoloza mapepala omwe athandizire pa kupezeka kwa ndalamazi
Read also: Dy/Dx expresses caution and support for Dr. Kabambe on Politics and Ideology WhatsApp Platform
Read also: Kamphangala reports to Chakwera AIP benefiting urban MCP members
Read also: Who else if not Wanderers’ BWEDE?
Boma la Malawi linabetsa ndalama zokwana K 750 million ku kampani ya Barkaat Foods Limited yomwe inkati igulitsa unduna wa zaulimi feteleza otsika mtengo
Lowe anatenga ndalama zokwana k30 Billion kupereka ku barkaat foods kuti agule fertilizer ndipo company ya barkaat foods inasowa ndi ndalamazo
Read also: Ngabu Sec School Sounds SOS
Read also: Criticism surrounds MCP media spokesperson Chawezi Banda
Read also: Stakeholders hail CEPPAM Projects





