FB IMG 1724506254258

Mtsogoleri wa timu ya Mighty Mukuru Wanderers a Thom Mpinganjira wati ndi wokondwa ndi m’mene timuyi ikuchitira pa masewero ake a mu ligi ya TNM.

A Mpinganjira ati apempha osewera a timuyi kuti adzipereke kwatunthu pa masewero omwe atsala nawo kuti apitilire kupereka mpikisano wa ukulu ku timu ya Silver Strikers yomwe ikutsogola pakadali pano.

Iwo ayamikiranso osewera wa pakati wa timuyi Isaac Kaliati kaamba komwetsa zigoli zisanu ndi zitatu mu ligiyi.

Wanderers ndi yachiwiri pa ndandanda wa matimu mu ligiyi ndi ma point 34 pamasewero 18 pomwe Silver ikutsogola ndi ma point 40 pamasewero 16.

Wolemba Peter Fote

Team manager wa Wanderers Steve Madeira kusangalala ndi Kaliati.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

See also  DPP Southern Region Governor Daud Chikwanje expresses gratitude to party for support after recent arrest

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *