UTM Ikutenga Boma Chaka Cha Mawa-Kaliati
Mlembi wamkuku wa UTM Mayi Kaliati ati UTM ikutenga boma chaka cha mawa.
Iwo ati boma la UTM likubwera kudzakonza chuma komanso kuthana ndi umphawi.Business sector gears up for UTM’s Mega Rally at Masintha Ground
Read also: What is wrong commemorating Chilima’s death concurrently at various venues?
Read also: Farming Not For Poor People-Chakwera
Read also: MPUC and Blantyre City Council to establish city peace and unity committees ahead of 2025 elections
A Kaliati pa msonkhanowu akukamba za momwe chuma cha dziko lino chayendera kuchoka m’zaka za mma 1980 kufika pano, pogwiritsa ntchito mbiri ya chuma yomwe ikuonetsedwa pa kanema wamkuluChrissy Kanyasho Declares Tonse Alliance Defunct; UTM MPs Now in Opposition.
Iwo adzudzula kuyendayenda kunja kwa mtsogoleri wa dziko lino pa nthawi yomwe Amalawi akuvutika ndi umphawi.
Read also: Lawyer and human rights advocate Alexius Kamangila issues warning: ‘FAKE page alert, be vigilant’
Read also: Police Nab Mutharika’s Stepson Tadikira
Read also: MIM Graduates 424





