FB IMG 1726433039248

A Chakwera Adzudzula Ogwiritsa ntchito imfa ya Chilima pa ndale

Mtsogoleri wa chipani cha MCP Dr. Lazarus Chakwera wadzudzula omwe akumalowetsa imfa ya wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino wakale Dr. Saulos Chilima munkhani za ndale.

Iwo ati anthu atenge zomwe zidatuluka mulipoti la akatswiri am’dziko la Germany komanso madotolo a m’dziko muno zokhudza ngozi ya ndege yomwe idapha a Chilima ndi anthu ena 8.

Mtsogoleriyu wati iwo ndi a Chilima anagwilizana zopanga ndale zotukula miyoyo ya a Malawi osati ndale zopakana matope.

Iwo ati ndi mtsogoleri yemwe wachita zitukuko zosiyanasiyana m’dziko muno ndipo athokoza anthu achipanichi powapasanso mwayi oti apitilize kutsogolera chipanichi.

More From Author

FB IMG 1726431828626 300x200

Former DPP SG Grezelder Jeffrey, Dr. Ntaba, others join ruling party

FB IMG 1726433440461 300x225

Mwanamveka Criticize Chakwera Led Government

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ella Brown

Project Manager

Darkness cannot drive out darkness; only light can do that. Hate cannot drive out hate: only love can do that.