Anzake kunjaku ndi a church omwenso amadalira kupempha.
President wakale wa dziko lino Mai Joyce Banda ati Dr Lazarus McCarthy Chakwera alibe network ya maiko akunja nkana mafuta ndi forex zikusowa mdziko muno.
Read also: Consult Before Appointments, Govt Warned
Read also: No Marburg Case Yet – Kayira
Read also: Chakwera bids Chitsulo farewell
Iwo amayankhula izi pa pulogalamu ya Kwagwanji pa Times Tv ndi anyamata atatu,Brian Banda, Wonder Msiska komanso Jonna Mpakuku.
Mai Banda adapitiliza kunena kuti mdziko lino liri pa moto wadzaoneni chifukwa a Chakwera alibe maubale ndi ma President akunja (Network alibe) choncho mafuta avutabe.
Read also: SA founded Fintech omniscient secures $7.5 million investment from arise
Read also: Jumbe says 16th September elections is about life or deaths
Read also: Nsanje District Council Loses Forgery Cases Against Former Accounts Assistant