Sindingapepese chifukwa Dambwe ndi malo Amizimu Yakufa, Nanga Ndikapepese ziwanda? – Enock Kanzingeni Chihana

“Sindingawope chifukwa ndimayankhulira aMalawi osauka komanso chipani!

Ulamuliro opanda masomphenya omwe ukutsogozedwa ndi mizimu yoyipa ukuyesera kuzunza anthu osalakwa kuti ukachite ufumu pamaso pa amphawi mu dziko la democracy!

Dambwe ndi malo a mizimu yakufa osati anthu amoyo!

Aliyense oyankhula m’malo mwa ziwanda sachita cholungama konse.

Ngati ndalakwira mizimu ndipo iyo imamva nayiyankhula iloreni tiyankhulane koma sindingapepetse munthu otumikira chinthu chopanda moyo!

Nanenso ndine mchewa ndipo tanthawuzo loti ndabwe ndimaliziwa kuti ndi dziko la mizimu yopanda moyo.

Ndikunenetsa molimba mtima mu dzina la YESU MKHRISTU mwana wa MULUNGU WAMOYO kuti sindingapepetse mizimu yopanda moyo chifukwa iyo ikuyenera kupita ku chiwonongeko pamodzi ndi ntchito zake zoyipa.

Related Posts

Step 30 International Ministries Brings Life-giving Water To Chingala Village

By Mabvuto Kalawa, Malawi Freedom Network Correspondent In a remarkable display of compassion and community development, Step 30 International Ministries has drilled a solar-powered borehole in Chingala Village, Lilongwe District,…

Redson Munlo Quits MCP, Cites Personal Decision Amid Growing Party Discontent

By Suleman Chitera Redson Munlo, a well-known political activist and member of the Malawi Congress Party (MCP), has resigned from the party, marking yet another high-profile exit at a time…

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

//otieu.com/4/9370459