Nduna yowona zokopa alendo yomwenso ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa chipani cha UTM, Michael Usi awuza President Lazarus chakwera kuti chipani cha UTM chilibe lingaliro lotuluka mu mgwilizano wa Tonse alliance ngakhale pali kagulu kena komwe kakufuna zinthu zitero.
A Usi ati kukakamiza chipani cha UTM kutuluka mu mgwilizano wa Tonse mchimodzimodzi kukakamiza munthu kuti atsike mu bwato lili pakati pa nyanja.
A Usi alumbila ponena kuti UTM ipitiliza kulemekeza mgwilizano wa Tonse.
Read also: Mass student expulsion rocks University of Malawi: 24 students kicked out for academic misconduct
Read also: Retired soldiers warn against politicized security forces: A threat to national stability
Read also: Jumbe says political agreements are not mere signatures on paper
Iwo ayankhula izi pa mwambo okumbukira mtsogoleri oyamba wa dziko lino Dr Hastings Kamuzu Banda Ku Lilongwe.
Poyankhulapo, ndunayi inauzanso Dr chakwera kuti achotse ntchito kagulu kena ka anthu komwe kakufuna kusokoneza boma lake.
Read also: Malawi Law Society Speaks Out on Allegations Against Justice Kenan Manda
Read also: Simeon super power Tchetha defeats Hannock Phiri in non-title encounter
Read also: FCB invests K183 million in BSC golf-course infrastructure