Katswili yemwe wachoka kumene kutimu ya Mighty Mukuru Wanderers Fc Yamikani Chester, akuyembekezereka kusaina m’gwilizano ndi timu ya Nyasa Big Bullets nthawi ina iliyonse.
Malingana ndi mphekesera zomwe wailesi ino yapeza, osewerayu wamvana ndi akuluakulu ena atimu ya Nyasa Big Bullets ndipo aphunzitsi ena atimuyi auzaso akuluakulu kuti asaine osewerayu asanapite ku timu ina.
Chester sanamvane ndi timu yake ya manoma pankhani yokhudza ndalama.
Read also: Police Assault Allegations in Dedza Spark Calls for Independent Investigation
Read also: Mutharika Assures IMF of Swift Action to Resolve Malawi’s Economic Crisis
Yamikani Ma Busy Chester akhala akukumana ndi akuluakulu oyendetsa timu ya Nyasa Big Bullets posachedwapa.
Read also: Creck Sporting, Blue Eagles Share Spoils in TNM Super League Clash at Aubrey Dimba Stadium
Read also: Multi Billion Theft And Cashgate On Kenyatta Road Project
Read also: Ministry of Agriculture to Strengthen Agricultural Loan Program for Small-Scale Farmers





