Mlembi wamkulu wa chipani cha PP Mr Chikhame wati chimanga chomwe boma la Malawi likugawa chabwera chifukwa Cha mtsogoleri wa chipani cha PP Dr Joyce Banda.
Iwo ati chimangachi chinachokela ku dziko la Ukraine chifukwa champando omwe mtsogoleri wawo anapasidwa ndi mtsogoleri wa Ukraine ngati Ambassador.
Read also: How Are We Going To Share Profits? -Zamba
Read also: Israel deploys multilayered missile defense system
Read also: Encourage Malawians to access NEEF loans-Usi
Iwo achenjedza chipani Cha MCP kuti chileke kugwiritsa ntchito chimanga Cha Ukraine ngati campaign chifukwa chinabwera kuno pansi pautsogoleri wa mayi Dr Joyce Banda.
Iwo aonjezelatso kuti chipani cha PP chizayima pa choka mchisankho Cha mawa. Iwo ati a Banda akhala akulangiza boma la a Chakwera koma sakumva malangizo a Dr Banda.
Read also: Political violence spreads as MCP-led government fails to condemn perpetrators
Read also: Huawei to Train 500 Young Malawians in Advanced ICT Skills to Drive MW2063 Agenda
Read also: CISONECC urges communities to adopt clean and renewable energy sources in the country





