IMG 20241110 WA0052

Mlembi wamkulu wa chipani cha PP Mr Chikhame wati chimanga chomwe boma la Malawi likugawa chabwera chifukwa Cha mtsogoleri wa chipani cha PP Dr Joyce Banda.

Iwo ati chimangachi chinachokela ku dziko la Ukraine chifukwa champando omwe mtsogoleri wawo anapasidwa ndi mtsogoleri wa Ukraine ngati Ambassador.

Iwo achenjedza chipani Cha MCP kuti chileke kugwiritsa ntchito chimanga Cha Ukraine ngati campaign chifukwa chinabwera kuno pansi pautsogoleri wa mayi Dr Joyce Banda.

Iwo aonjezelatso kuti chipani cha PP chizayima pa choka mchisankho Cha mawa. Iwo ati a Banda akhala akulangiza boma la a Chakwera koma sakumva malangizo a Dr Banda.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

See also  Dr. Joyce Banda announces plans for free secondary education upon returning to power

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *