Friday, June 9Malawi's top news source
Shadow

APOLISI AMANGA NURSE KAMBA KONYOZA CHAKWERA PA WHATSAPP

A Malawi Police amanga nurse wa chipatala cha Ntcheu District Hospital, a Chidawawa Mainje, a dzaka zakubadwa 39 powaganizira kuti ananyoza mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera kudzera pa tsamba la mchezo la Whatsapp.
News update
Yapeza kuti a Mainje amachita mtsuso (debate) ndi anzawo pa whatsapp group. Mtsusowo unali wa ndale, okamba za momwe zinthu zikuyendera m’dziko muno mu ulamuliro wa Lazarus Chakwera ndi wachiwiri wake, Saulos Chilima.

Mtsusowo unakolera moto, ndipo Mainje anatemetsa nkhwangwa pa mwala kuti zinthu siziri bwino m’dziko muno, ndipo Chakwera walephera kuyendetsa dziko lino ngati mtsogoleri.

Ali mkati mwa mtsusowo, munthu wina pa group-yo anajambura (screenshot) zomwe anayankhura Mainje, ndipo adadziwitsa mkulu wina wa boma la Chakwera.

Mkuluyo atawona ma screenshot-wo anakwiya kwambiri, ndipo posakhalitsa galimoto ya police inabwera kuchokera komwe ku likulu la police ku area 30 mu mzinda wa Lilongwe, ndipo linamanga Mainje.

Related News
NEEF Customers Demands Their Deposit Back

A group of business people who applied for National Economic Empowerment Fund (Neef) loans in Mzuzu tstormed office premises for Read more

Police move to protect persons with albinism

Malawi Police Service has engaged traditional healers in Mwanza on how to protect persons with albinism in the district. Speaking Read more

MARTHA CHIZUMA DECLARES WAR AGAINST CHAKWERA: SAYS PRESIDENT, JUDICIARY, ARMY AND POLICE CORRUPT

In a shocking tale to absorb, ACB boss Martha Chizuma has taken her corruption fight against her bosses, openly going Read more

Police in Chitipa district have arrested Kayange who poured hot water on her husband

According to Chitipa Police PRO Gladwell Simwaka, on March 7, 2022 the victim Blair Kuyokwa, 35, returned home in the Read more

Lilongwe Police recover stolen items

Police in Lilongwe have for the second time this month recovered household items and other property worth over 23 million Read more

Police at Bangwe in Blantyre have arrested three suspects

*Police at Bangwe in Blantyre have arrested three suspects and recovered some items they allegedly stole at Namiyango Assemblies of Read more

CSO SPEAKS AGAINST Anti-Ashok Nair Demos: Says they are ‘Criminal’ in Nature

The Citizen Advancement for Economic Revolution has described the anti-Ashok Nair demonstrations scheduled for tomorrow Wednesday as criminal in nature. Read more

M’tengo wa pakete imodzi ya shuga, tsopano ukumafanana ndi wa bread m’modzi

Izi zadza chifukwa bread wakwela mtengo kufika pa 1 000 Kwacha m'modzi , m'magolosale ena. Akuluakulu ena omwe ali ndi Read more

Police Summon Gaffar Over Death Threats

Details have emerged indicating that Malawi Police has summoned Rafik Gaffar of R Gaffar Transport for series of death threats Read more

?ife ?ollows ?usband ?o ?rison ?or ?ermitting ?efilement ?f ?er ?aughter

A 36-year old mother Maimuna Kassim who hails from Mikundi Village in the area of Traditional Authority Mponda, in Mangochi Read more

News To Read

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *